Yakobo 2:20 - Buku Lopatulika20 Koma ufuna kuzindikira kodi, munthu wopanda pake iwe, kuti chikhulupiriro chopanda ntchito chili chabe? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Koma ufuna kuzindikira kodi, munthu wopanda pake iwe, kuti chikhulupiriro chopanda ntchito chili chabe? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Wopusawe, kodi ukufuna umboni wotsimikiza kuti chikhulupiriro chopanda ntchito zake nchachabe? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Munthu wopusa iwe, kodi ukufuna umboni woti chikhulupiriro chopanda ntchito zabwino nʼchakufa? Onani mutuwo |