Yakobo 2:15 - Buku Lopatulika15 Mbale kapena mlongo akakhala wausiwa, ndi kusowa chakudya cha tsiku lake, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Mbale kapena mlongo akakhala wausiwa, nichikamsowa chakudya cha tsiku lake, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Mwachitsanzo: mbale wina kapena mlongo ali ndi usiŵa, ndipo masiku onse alibe chakudya chokwanira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Tangoganizirani, mʼbale kapena mlongo amene ali ndi usiwa, ndipo alibe chakudya cha tsiku ndi tsiku. Onani mutuwo |