Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yakobo 1:20 - Buku Lopatulika

20 Pakuti mkwiyo wa munthu suchita chilungamo cha Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Pakuti mkwiyo wa munthu suchita chilungamo cha Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Paja munthu wokwiya safikapo pa chilungamo chimene amafuna Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Pakuti mkwiyo wa munthu subweretsa chilungamo chimene amafuna Mulungu.

Onani mutuwo Koperani




Yakobo 1:20
5 Mawu Ofanana  

koma Ine ndinena kwa inu, kuti yense wokwiyira mbale wake wopanda chifukwa adzakhala wopalamula mlandu; ndipo amene adzanena ndi mbale wake, Wopanda pake iwe, adzakhala wopalamula mlandu wa akulu: koma amene adzati, Chitsiru iwe: adzakhala wopalamula Gehena wamoto.


Kwiyani, koma musachimwe; dzuwa lisalowe muli chikwiyire,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa