Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Tito 3:15 - Buku Lopatulika

15 Akukupatsa moni onse akukhala pamodzi ndi ine. Pereka moni kwa otikondawo m'chikhulupiriro. Chisomo chikhale ndi inu nonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Akukupatsa moni onse akukhala pamodzi ndi ine. Pereka moni kwa otikondawo m'chikhulupiriro. Chisomo chikhale ndi inu nonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Onse amene ali nane kuno akuti moni. Uperekeko moni kwa onse amene amatikonda chifukwa cha chikhulupiriro. Mulungu akukomereni mtima nonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Onse amene ali ndi ine akupereka moni. Upereke moni kwa amene amatikonda ife mʼchikhulupiriro. Chisomo chikhale ndi inu nonse.

Onani mutuwo Koperani




Tito 3:15
14 Mawu Ofanana  

Ndipo ngati mupatsa moni abale anu okhaokha, muchitanji choposa ena? Kodi angakhale anthu akunja sachita chomwecho?


Mudziwa inu nokha kuti manja anga awa anatumikira zosowa zanga, ndi za iwo akukhala ndi ine.


Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu chikhale ndi inu.


Pakuti mwa Khristu Yesu kapena mdulidwe kapena kusadulidwa kulibe mphamvu; komatu chikhulupiriro, chakuchititsa mwa chikondi.


Ndipereka moni ndi dzanja langa, kwa ine Paulo. Kumbukirani zomangira zanga. Chisomo chikhale nanu.


kwa Timoteo mwana wanga weniweni m'chikhulupiriro: Chisomo, chifundo, mtendere za kwa Mulungu Atate ndi kwa Khristu Yesu Ambuye wathu.


koma chitsirizo cha chilamuliro ndicho chikondi chochokera mu mtima woyera ndi m'chikumbu mtima chokoma ndi chikhulupiriro chosanyenga;


Ambuye akhale ndi mzimu wako. Chisomo chikhale nanu.


pakumva za chikondi chako ndi chikhulupiriro uli nacho chakulinga kwa Ambuye Yesu, ndi kwa oyera mtima onse;


Chisomo chikhale ndi inu nonse, Amen.


Mkuluyo kwa Gayo wokondedwayo, amene ndikondana naye m'choonadi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa