Tito 1:14 - Buku Lopatulika14 osasamala nthano zachabe za Chiyuda, ndi malamulo a anthu opatuka kusiyana nacho choonadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 osasamala nthano zachabe za Chiyuda, ndi malamulo a anthu opatuka kusiyana nacho choonadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 m'malo momasamala nthano zachiyuda, ndi malamulo a anthu okana choona. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 kuti asasamalenso nthano za Chiyuda, ndi malamulo a anthu amene akukana choonadi. Onani mutuwo |