Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Rute 4:22 - Buku Lopatulika

22 ndi Obedi anabala Yese, ndi Yese anabala Davide.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 ndi Obedi anabala Yese, ndi Yese anabala Davide.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Obedi adabereka Yese ndipo Yese adabereka Davide.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Obedi anali abambo a Yese, ndipo Yese anali abambo a Davide.

Onani mutuwo Koperani




Rute 4:22
10 Mawu Ofanana  

ndi Bowazi anabala Obedi, ndi Obedi anabala Yese,


Ozemu wachisanu ndi chimodzi, Davide wachisanu ndi chiwiri;


Ndipo padzatuluka mphukira pa tsinde la Yese, ndi nthambi yotuluka m'mizu yake idzabala zipatso;


ndi Yese anabala Davide mfumuyo. Ndipo Davide anabala Solomoni mwa mkazi wa Uriya;


mwana wa Melea, mwana wa Mena, mwana wa Matata, mwana wa Natamu, mwana wa Davide,


Ndi akazi anansi ake anamutcha dzina, ndi kuti, Kwa Naomi kwambadwira mwana; namutcha dzina lake Obedi; ndiye atate wa Yese atate wa Davide.


ndi Salimoni anabala Bowazi, ndi Bowazi anabala Obedi;


Ndipo panali munthu wina wa ku Ramatayimu Zofimu, wa dziko la mapiri la Efuremu, dzina lake ndiye Elikana, mwana wake wa Yerohamu, mwana wa Elihu, mwana wa Tohu, mwana wa Zufu, Mwefuremu.


Ndipo Yehova ananena ndi Samuele, Iwe ukuti ulire chifukwa cha Saulo nthawi yotani, popeza Ine ndinamkana kuti asakhale mfumu ya Israele? Dzaza nyanga yako ndi mafuta, numuke, ndidzakutumiza kwa Yese wa ku Betelehemu; pakuti ndinadzionera mfumu pakati pa ana ake.


Tsono Davide anali mwana wa Mwefurati uja wa ku Betelehemu ku Yuda, dzina lake ndiye Yese; ameneyu anali nao ana aamuna asanu ndi atatu; ndipo m'masiku a Saulo munthuyo anali nkhalamba, mwa anthu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa