Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Rute 4:19 - Buku Lopatulika

19 ndi Hezironi anabala Ramu, ndi Ramu anabala Aminadabu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 ndi Hezironi anabala Ramu, ndi Ramu anabala Aminadabu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Hezironi adabereka Ramu, Ramu adabereka Aminadabu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Hezironi anali abambo a Ramu, Ramu anali abambo a Aminadabu,

Onani mutuwo Koperani




Rute 4:19
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Aroni anadzitengera Eliseba, mwana wamkazi wa Aminadabu, mlongo wake wa Nasoni, akhale mkazi wake; ndipo anambalira Nadabu ndi Abihu, Eleazara ndi Itamara.


ndi Ramu anabala Aminadabu; ndi Aminadabu anabala Nasoni; ndi Nasoni anabala Salimoni;


mwana wa Aminadabu, mwana wa Admini, mwana wa Arini, mwana wa Hezironi, mwana wa Perezi, mwana wa Yuda,


Iyo ndiyo mibadwo ya Perezi; Perezi anabala Hezironi;


ndi Aminadabu anabala Nasoni, ndi Nasoni anabala Salimoni;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa