Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Rute 3:17 - Buku Lopatulika

17 Natinso, Miyeso iyi isanu ndi umodzi ya barele anandipatsa, pakuti anati, Usafike kwa mpongozi wako wopanda kanthu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Natinso, Miyeso, iyi isanu ndi umodzi ya barele anandipatsa, pakuti anati, Usafike kwa mpongozi wako wopanda kanthu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 ndipo adati, “Wandipatsa makilogramu makumi aŵiri a barele, nandiwuza kuti, ‘Usapite kwa apongozi ako chimanjamanja.’ ”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Ndipo anati, “Munthuyo anandipatsa makilogalamu makumi awiri awa a barele, nandiwuza kuti usapite kwa apongozi ako wopanda kanthu.”

Onani mutuwo Koperani




Rute 3:17
2 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene anadza kwa mpongozi wake, iye anati, Wapeza bwanji, mwana wanga? Pamenepo anamfotokozera zonse anamchitira munthuyo.


Ndipo anati, Khala ulipo, mwana wanga, mpaka udziwa umo ukhalire mlandu; pakuti munthuyo sadzauleka mpaka atautha mlanduwo lero lino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa