Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Rute 2:21 - Buku Lopatulika

21 Ndipo Rute Mmowabu anati, Ananenanso nane ndithu, Uwaumirire anyamata anga, mpaka atatha kucheka zanga zonse za m'minda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Ndipo Rute Mmowabu anati, Ananenanso nane ndithu, Uwaumirire anyamata anga, mpaka atatha kucheka zanga zonse za m'minda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Tsono Rute Mmowabuyo adati, “Kuwonjezera pamenepo, munthuyo anandiwuza kuti, ‘Uzitsata antchito angaŵa mpaka atamaliza munda wanga kukolola.’ ”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Choncho Rute Mmowabuyo anati, “Iye anandiwuzanso kuti, ‘Uzitsata antchito angawa mpaka atamaliza kukolola munda wonse.’ ”

Onani mutuwo Koperani




Rute 2:21
4 Mawu Ofanana  

Nati Naomi kwa mpongozi wake, Yehova amdalitse amene sanaleke kuwachitira zokoma amoyo ndi akufa. Ndipo Naomi ananena naye, Munthuyo ndiye mbale wathu, ndiye mmodzi wa iwo otiombolera cholowa.


Nati Naomi kwa Rute mpongozi wake, Nchabwino, mwana wanga, kuti uzituluka nao adzakazi ake, ndi kuti asakukomane m'munda wina uliwonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa