Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Rute 2:18 - Buku Lopatulika

18 nalisenza nalowa kumzinda; ndipo mpongozi wake anaona khunkhalo; Rute natulutsanso nampatsa mkute uja anausiya atakhuta.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 nalisenza nalowa kumudzi; ndipo mpongozi wake anaona khunkhalo; Rute natulutsanso nampatsa mkute uja anausiya atakhuta.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Adatenga bareleyo kupita naye ku mudzi, nakaonetsa mpongozi wake. Atatero, adatulutsa chakudya chimene chidatsalira atakhuta chija, napatsa mpongozi wakeyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Anasenza barele uja kupita naye ku mudzi, nakaonetsa apongozi ake. Kenaka anatulutsa chakudya chimene chinatsalira atakhuta chija ndi kupatsa apongozi ake.

Onani mutuwo Koperani




Rute 2:18
4 Mawu Ofanana  

Koma ngati wamasiye wina ali nao ana kapena adzukulu, ayambe aphunzire iwo kuchitira ulemu a m'banja lao, ndi kubwezera akuwabala; pakuti ichi ncholandirika pamaso pa Mulungu.


Ndipo pa nthawi ya kudya Bowazi ananena naye, Sendera kuno, nudyeko mkate; nusunse nthongo yako m'vinyo wosasayo. Nakhala iye m'mbali mwa ochekawo; ndipo anamtambasulira dzanja kumninkha tirigu wokazinga, nadya iye, nakhuta, nasiyapo.


Natola khunkha iye m'munda mpaka madzulo; naomba khunkhalo; napeza ngati efa wa barele,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa