Rute 2:13 - Buku Lopatulika13 Nati iye, Mundikomere mtima mbuye wanga, popeza mwandisangalatsa, popezanso mwanena chokondweretsa mtima wa mdzakazi wanu, ndingakhale ine sindine ngati mmodzi wa adzakazi anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Nati iye, Mundikomere mtima mbuye wanga, popeza mwandisangalatsa, popezanso mwanena chokondweretsa mtima wa mdzakazi wanu, ndingakhale ine sindine ngati mmodzi wa adzakazi anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Apo Rute adati, “Mwandikomera mtima kwambiri mbuyanga, mwandisangalatsa ndipo mwandilankhula mwachifundo, ngakhale sindine mmodzi mwa adzakazi anu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Rute anati, “Mwandikomera mtima, mbuye wanga. Ndipo mwandisangalatsa ndi kundiyankhula mwa chifundo ngakhale sindili mmodzi mwa adzakazi anu.” Onani mutuwo |