Rute 1:20 - Buku Lopatulika20 Koma ananena nao, Musanditcha Naomi, munditche Mara; pakuti Wamphamvuyonse anandichitira zowawa ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Koma ananena nao, Musanditcha Naomi, munditche Mara; pakuti Wamphamvuyonse anandichitira zowawa ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Iyeyo adaŵauza kuti, “Musamanditchule Naomi, koma muzinditchula Mara, poti Mphambe wandizunza kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Iye anawawuza kuti, “Musanditchenso Naomi. Muzinditchula ine kuti Mara, chifukwa Wamphamvuzonse wandizunza kwambiri. Onani mutuwo |