Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Rute 1:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo pakuona kuti analimbika kumuka naye, analeka kulankhula naye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo pakuona kuti analimbika kumuka naye, analeka kulankhula naye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Naomi ataona kuti Rute watsimikiza kupita nao, sadanenenso kanthu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Naomi atazindikira kuti Rute watsimikiza kupita naye, analeka kumukakamiza.

Onani mutuwo Koperani




Rute 1:18
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anali chikhalire m'chiphunzitso cha atumwi ndi m'chiyanjano, m'kunyema mkate ndi mapemphero.


Ndipo pokana iye kukopeka, tinaleka, ndi kuti, Kufuna kwa Ambuye kuchitidwe.


Chotsalira, tadzilimbikani mwa Ambuye, ndi m'kulimba kwa mphamvu yake.


Namuka iwo awiriwo mpaka anafika ku Betelehemu. Ndipo kunali pakufika iwo ku Betelehemu, mudzi wonse unapokosera za iwo; nati, Kodi uyu ndi Naomi?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa