Rute 1:17 - Buku Lopatulika17 kumene mudzafera inu ine ndidzafera komweko, ndi kuikidwa komweko; andilange Yehova naonjezeko, chilichonse chikasiyanitsa inu ndi ine, koma imfa ndiyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 kumene mudzafera inu ine ndidzafera komweko, ndi kuikidwa komweko; andilange Yehova naonjezeko, chilichonse chikasiyanitsa inu ndi ine, koma imfa ndiyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Kumene inu mukafere, inenso ndikafera komweko ndi kuikidwa komweko. Chauta andichite choipa chilichonse chingakule motani, ngati kanthu kena kalikonse katisiyanitse, kupatula imfa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Kumene mukafere inenso ndidzafera komweko ndipo komweko ndikayikidwa mʼmanda. Yehova andichite choyipa chingakule motani, ngati china chingatirekanitse ife kupatula imfa.” Onani mutuwo |