Rute 1:15 - Buku Lopatulika15 Pamenepo anati, Taona mbale wako wabwerera kwa anthu a kwao, ndi kwa mulungu wake, bwerera umtsate mbale wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Pamenepo anati, Taona mbale wako wabwerera kwa anthu a kwao, ndi kwa mulungu wake, bwerera umtsate mbale wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Tsono Naomi adauza Rute kuti, “Ona, mbale wako wabwerera kwao ndi kwa milungu yake. Nawenso bwerera, umulondole mbale wakoyo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Naomi anati “Taona, mʼbale wako wabwerera kwawo kwa anthu ake ndi kwa milungu yake. Bwerera nawenso umulondole mʼbale wako.” Onani mutuwo |