Rute 1:14 - Buku Lopatulika14 Nakweza iwo mau ao, naliranso misozi; ndi Oripa anampsompsona mpongozi wake, koma Rute anamkangamira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Nakweza iwo mau ao, naliranso misozi; ndi Oripa anampsompsona mpongozi wake, koma Rute anamkangamira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Pamenepo iwo aja adayambanso kulira mokweza. Olipa adampsompsona mpongozi wake ndi kumulaŵira, koma Rute adakangamira Naomiyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Atamva zimenezi analiranso kwambiri, ndipo Oripa anapsompsona apongozi ake nawatsanzika, koma Rute anakakamirabe. Onani mutuwo |