Oweruza 9:8 - Buku Lopatulika8 Kumuka inamuka mitengo kudzidzozera mfumu; niti kwa mtengo wa azitona, Ukhale iwe mfumu yathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Kumuka inamuka mitengo kudzidzozera mfumu; niti kwa mtengo wa azitona, Ukhale iwe mfumu yathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Padangotere: mitengo idapita kukalonga mfumu yoti iziilamulira. Ndiye mitengoyo idauza mtengo wa olivi kuti, ‘Iwe ukhale mfumu yathu.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Tsiku lina mitengo inapita kukadzoza mfumu yawo. Tsono mitengoyo inati kwa mtengo wa olivi, ‘Iwe ukhale mfumu yathu.’ ” Onani mutuwo |