Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Oweruza 8:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo ananenanso kwa amuna a ku Penuwele ndi kuti, Ndikabwerera ndi mtendere ndidzagumula nsanja iyi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo ananenanso kwa amuna a ku Penuwele ndi kuti, Ndikabwerera ndi mtendere ndidzagumula nsanja iyi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Apo Gideoni adauza anthu a ku Penuwele kuti, “Pamene ndizikabwerera nditagonjetsa, ndidzagwetsa nsanja ili apayi.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Gideoni anawawuzanso kuti, “Ndikamadzabwerera nditawagonjetsa, ndidzagwetsa nsanja iyi.”

Onani mutuwo Koperani




Oweruza 8:9
3 Mawu Ofanana  

Zeba ndi Zalimuna ndipo anali mu Karikori, ndi a m'misasa ao pamodzi nao, amuna monga zikwi khumi ndi zisanu; ndiwo otsala onse a khamu lonse la ana a kum'mawa; popeza atagwa amuna zikwi zana limodzi ndi makumi awiri akusolola lupanga.


Ndipo anagamula nsanja ya Penuwele, napha amuna akumzinda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa