Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Oweruza 8:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo Gideoni anati, Chifukwa chake, Yehova akapereka Zeba ndi Zalimuna m'dzanja langa, ndidzapuntha nyama yanu ndi minga ya m'chipululu ndi mitungwi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo Gideoni anati, Chifukwa chake, Yehova akapereka Zeba ndi Zalimuna m'dzanja langa, ndidzapuntha nyama yanu ndi minga ya m'chipululu ndi mitungwi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Gideoni adayankha kuti, “Ai, chabwino! Chauta akapereka Zeba ndi Zalimuna m'manja mwanga, ndidzakukwapulani ndi matsatsa a minga yam'chipululu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Gideoni anayankha kuti, “Mwatero! Yehova akapereka Zeba ndi Zalimuna mʼdzanja langa, ndidzakukwapulani ndi matsatsa a minga ya mʼchipululu.”

Onani mutuwo Koperani




Oweruza 8:7
2 Mawu Ofanana  

Ndipo kunali, pakumva Gideoni kufotokozera kwa lotolo ndi tanthauzo lake, anadziwerama; nabwera ku misasa ya Israele nati, Taukani, pakuti Yehova wapereka a m'misasa a Midiyani m'dzanja lanu.


Ndipo ananena kwa amuna a ku Sukoti, Mupatsetu anthu awa akunditsata mitanda yamkate; pakuti atopa, ndipo ndilikulondola Zeba ndi Zalimuna mafumu a Midiyani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa