Oweruza 8:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo Gideoni anafika ku Yordani, naoloka, iye ndi amuna mazana atatu anali naye, ali otopa koma ali chilondolere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo Gideoni anafika ku Yordani, naoloka, iye ndi amuna mazana atatu anali naye, ali otopa koma ali chilondolere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Gideoni adafika ku Yordani naoloka mtsinjewo, iye pamodzi ndi anthu 300 aja amene nali nawo, atatopa kwambiri, koma akupirikitsabe adani ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Gideoni anafika ndi kuwoloka mtsinje wa Yorodani pamodzi ndi anthu 300 amene anali naye. Ngakhale kuti anali otopa anapirikitsabe adani awo. Onani mutuwo |