Oweruza 8:3 - Buku Lopatulika3 Mulungu anapereka m'dzanja lanu akalonga a Midiyani, Orebu ndi Zeebu, ndipo ndinakhoza kuchitanji monga inu? Pamenepo mkwiyo wao unamlezera, atanena mau awa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mulungu anapereka m'dzanja lanu akalonga a Midiyani, Orebu ndi Zeebu, ndipo ndinakhoza kuchitanji monga inu? Pamenepo mkwiyo wao unamlezera, atanena mau awa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mulungu wapereka m'manja mwanu mafumu a Midiyani, Orebu ndi Zebu. Ndachita chiyani kuyerekeza ndi zimene mwachita inu?” Gideoni atanena mau amenewo, anthuwo mitima yao idatsika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mulungu wapereka mafumu a Midiyani, Orebu ndi Zeebu mʼmanja mwanu. Ndachita chiyani kuyerekeza ndi zimene mwachita inu?” Atanena izi, anthuwo mitima yawo inatsika. Onani mutuwo |