Oweruza 8:2 - Buku Lopatulika2 Koma ananena nao, Ndachitanji tsopano monga inu? Kodi kukunkha mphesa kwa Efuremu sikuposa kutchera mphesa kwa Abiyezere? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Koma ananena nao, Ndachitanji tsopano monga inu? Kodi kukunkha mphesa kwa Efuremu sikuposa kutchera mphesa kwa Abiyezere? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Iye adaŵayankha kuti, “Ndachita chiyani ine kuyerekeza ndi zimene mwachita inu? Kodi zimene mwachita inu Aefuremu si zazikulu koposa zimene fuko langa la Abiyezere lachita? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Koma iye anawayankha kuti, “Nʼchiyani ndachita kuyerekeza ndi zimene mwachita inu? Kodi zimene mwachita inu Aefereimu si zazikulu kuposa zimene fuko langa la Abiezeri lachita? Onani mutuwo |