Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Oweruza 8:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo Zeba ndi Zalimuna anathawa; koma anawatsata, nagwira mafumu awiri a Midiyani Zeba ndi Zalimuna, nanjenjemeretsa khamu lonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo Zeba ndi Zalimuna anathawa; koma anawatsata, nagwira mafumu awiri a Midiyani Zeba ndi Zalimuna, nanjenjemeretsa khamu lonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Zeba ndi Zalimuna adathaŵa. Gideoni adaŵapirikitsa nagwira mafumu aŵiri a Midiyaniwo, ndipo ankhondo ao onse adathaŵa ndi mantha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Zeba ndi Zalimuna, mafumu awiri a Amidiyani anathawa koma Gideoni anawathamangitsa mpaka kuwagwira. Koma ankhondo awo onse anathawa ndi mantha.

Onani mutuwo Koperani




Oweruza 8:12
12 Mawu Ofanana  

Nanga kwa Iye wosasamalira nkhope za akalonga, wosasiyanitsa pakati pa wolemera ndi wosauka? Pakuti onsewo ndiwo ntchito ya manja ake.


Muwaike akulu ao ngati Orebu ndi Zeebu; mafumu ao ngati Zeba ndi Zalimuna,


Inu mwachulukitsa mtundu, inu mwaenjezera kukondwa kwao; iwo akondwa pamaso panu monga akondwera m'masika, monga anthu akondwa pogawana zofunkha.


Ndipo populumukirapo padzasowera waliwiro, ndi wamphamvu; sadzalimbikitsa mphamvu yake, ndi ngwazi siidzapulumutsa moyo wake;


Ndinaona mahema a Kusani ali mkusauka; nsalu zotchinga za dziko la Midiyani zinanjenjemera.


Ndipo Gideoni anakwerera njira ya iwo okhala m'mahema kum'mawa kwa Noba, ndi Yogobeha, nakantha khamulo popeza khamulo linakhala lokhazikika mtima.


Pamenepo Gideoni mwana wa Yowasi anabwerera kunkhondo pokwerera pa Heresi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa