Oweruza 7:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo kunali usiku womwewo, kuti Yehova ananena naye, Tauka, tatsikira kumisasa; pakuti ndaipereka m'dzanja lako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo kunali usiku womwewo, kuti Yehova ananena naye, Tauka, tatsikira kumisasa; pakuti ndaipereka m'dzanja lako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Usiku womwewo Chauta adauza Gideoni kuti, “Dzuka, pita ukazithire nkhondo zithandozo, pakuti ndazipereka m'manja mwako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Usiku umenewo Yehova anati kwa Gideoni, “Dzuka, pita kachite nkhondo ku misasayo, chifukwa ndayipereka mʼmanja mwako. Onani mutuwo |