Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Oweruza 7:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo Yehova anati kwa Gideoni, Ndi anthu mazana atatu akukhatira ndidzakupulumutsani, ndi kupereka Amidiyani m'dzanja lako; koma amuke anthu awa onse, yense kumalo kwake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo Yehova anati kwa Gideoni, Ndi anthu mazana atatu akukhatira ndidzakupulumutsani, ndi kupereka Amidiyani m'dzanja lako; koma amuke anthu awa onse, yense kumalo kwake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Ndipo Chauta adauza Gideoni kuti, “Ndidzakupulumutsani ndi anthu 300 okhaŵa amene adakhathira pakumwa madzi, ndipo ndidzapereka Amidiyani m'manja mwako. Koma ena onsewo apite kwao.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Yehova anati kwa Gideoni, “Ndi anthu 300 amene anamwa madzi mokhathira ndi manja awo ndidzakupulumutsani ndipo ndidzapereka Amidiyani mʼmanja mwanu. Koma anthu ena onse apite ku nyumba kwawo.”

Onani mutuwo Koperani




Oweruza 7:7
6 Mawu Ofanana  

Ndi kuwerenga kwa iwo akukhatira, ndi kuika dzanja lao kukamwa kwao, ndiko mazana atatu; koma ena onse anagwada pakumwa madzi.


Pamenepo anthu anatenga kamba m'dzanja lao, ndi malipenga ao; ndipo anauza amuna onse a Israele amuke, yense kuhema kwake; koma anaimika amuna mazana atatuwo; ndipo misasa ya Midiyani inali kunsi kwake m'chigwa.


Ndipo Yonatani ananena ndi mnyamata wonyamula zida zake, Tiye tipite ku kaboma ka osadulidwa awa; kapena Yehova adzatigwirira ntchito; pakuti palibe chomletsa Yehova kupulumutsa angakhale ndi ambiri kapena ndi owerengeka.


Tsono Davide anafunsiranso kwa Yehova. Ndipo Yehova anamyankha iye, nati, Nyamuka, nutsikire ku Keila; pakuti ndidzapereka Afilisti m'dzanja lako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa