Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Oweruza 7:6 - Buku Lopatulika

6 Ndi kuwerenga kwa iwo akukhatira, ndi kuika dzanja lao kukamwa kwao, ndiko mazana atatu; koma ena onse anagwada pakumwa madzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndi kuwerenga kwa iwo akukhatira, ndi kuika dzanja lao kukamwa kwao, ndiko mazana atatu; koma ena onse anagwada pakumwa madzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Tsono chiŵerengero cha anthu amene adakhathira madzi pakumwa ndi manja chinali anthu 300. Koma anthu ena onse otsala adagwada pansi kuti amwe madzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Ndipo anthu 300 anamwa mokhathira, pamene ena onse anagwada pansi pakumwa.

Onani mutuwo Koperani




Oweruza 7:6
4 Mawu Ofanana  

Adzamwa kumtsinje wa panjira; chifukwa chake adzaweramutsa mutu wake.


Njira zonse za munthu ziyera pamaso pake; koma Yehova ayesa mizimu.


Ndipo anatsikira nao anthu kumadzi; ndipo Yehova anati kwa Gideoni, Aliyense akapiza madzi pa lilime lake, monga akhatira galu, ameneyo amuike pa yekha; momwemo aliyense agwada pakumwa.


Ndipo Yehova anati kwa Gideoni, Ndi anthu mazana atatu akukhatira ndidzakupulumutsani, ndi kupereka Amidiyani m'dzanja lako; koma amuke anthu awa onse, yense kumalo kwake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa