Oweruza 6:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo kunali, akabzala Israele, amakwera Amidiyani, ndi Amaleke, ndi ana a kum'mawa, inde amawakwerera; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo kunali, akabzala Israele, amakwera Amidiyani, ndi Amaleke, ndi ana a kum'mawa, inde amawakwerera; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Aisraele ankati akabzala mbeu, Amidiyani ndi Aamaleke pamodzi ndi anthu akuvuma, ankabwera kudzaŵathira nkhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Aisraeli amati akadzala mbewu, Amidiyani, Aamaleki ndi anthu ena akummawa amabwera ndi kudzawathira nkhondo. Onani mutuwo |