Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Oweruza 5:9 - Buku Lopatulika

9 Mtima wanga uvomerezana nao olamulira a mu Israele, amene anadzipereka mwaufulu mwa anthu. Lemekezani Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Mtima wanga uvomerezana nao olamulira a m'Israele, amene anadzipereka mwaufulu mwa anthu. Lemekezani Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Mtima wanga uli ndi atsogoleri a ankhondo a ku Israele, uli ndi anthu amene adadzipereka mwaufulu, kudzipereka mwaufulu pakati pa anzao. Tamandani Chauta!

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Mtima wanga uli ndi atsogoleri a Israeli, uli ndi anthu amene anadzipereka okha mwaufulu pakati pa anthu. Tamandani Yehova!

Onani mutuwo Koperani




Oweruza 5:9
11 Mawu Ofanana  

Ndipo anthu anakondwera popeza anapereka mwaufulu; pakuti ndi mtima wangwiro anapereka mwaufulu kwa Yehova; mfumu Davide yemwe anakondwera ndi chimwemwe chachikulu.


ndi wotsatana naye Amasiya mwana wa Zikiri, wodzipereka kwa Yehova mwaufulu, ndi pamodzi ndi iye ngwazi zamphamvu zikwi mazana awiri;


Ndipo pamene Hezekiya ndi akulu ake anadza, naona miyuluyi, analemekeza Yehova, nadalitsa anthu ake Aisraele.


Ndipo anthu anadalitsa amuna onse akudzinenera mwaufulu kuti adzakhala mu Yerusalemu.


Lemekeza Yehova, moyo wanga, ndi kusaiwala zokoma zake zonse atichitirazi:


Anthu anu adzadzipereka eni ake tsiku la chamuna chanu: M'moyera mokometsetsa, mobadwira matanda kucha, muli nao mame a ubwana wanu.


Pakuti ngati chivomerezocho chili pomwepo, munthu alandiridwa monga momwe ali nacho, si monga chimsowa.


Pakutitu analandira kudandaulira kwathu; koma pokhala nalo khama loposa, anatulukira kunka kwa inu mwini wake.


Chifukwa chake ndinayesa kuti kufunika kupempha abale kuti atsogole afike kwa inu, nakonzeretu dalitso lanu lolonjezeka kale, kuti chikhale chokonzeka chomwechi, monga ngati mdalitso, ndipo si monga mwa kuumiriza.


Lemekezani Yehova pakuti atsogoleri mu Israele anatsogolera, pakuti anthu anadzipereka mwaufulu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa