Oweruza 5:2 - Buku Lopatulika2 Lemekezani Yehova pakuti atsogoleri mu Israele anatsogolera, pakuti anthu anadzipereka mwaufulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Lemekezani Yehova pakuti atsogoleri m'Israele anatsogolera, pakuti anthu anadzipereka mwaufulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Pakuti atsogoleri adatsogoleradi m'dziko la Israele, ndipo anthu adadzipereka okha mwaufulu, tamandani Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Popeza kuti atsogoleri anatsogoleradi mʼdziko la Israeli; ndipo anthu anadzipereka okha mwa ufulu, tamandani Yehova: Onani mutuwo |