Oweruza 4:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo Baraki anati kwa iye, Ukamuka nane, ndidzamuka; ukapanda kumuka nane, sindimuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo Baraki anati kwa iye, Ukamuka nane, ndidzamuka; ukapanda kumuka nane, sindimuka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Baraki adayankha kuti, “Mukapita, nanenso ndipita, koma mukapanda kupita, inenso sindipita.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Baraki anamuyankha kuti, “Mukapita nane limodzi ine ndipita. Koma ngati sitipitira limodzi, inenso sindipita.” Onani mutuwo |