Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Oweruza 4:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo ana a Israele anaonjeza kuchita choipa pamaso pa Yehova, atafa Ehudi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo ana a Israele anaonjeza kuchita choipa pamaso pa Yehova, atafa Ehudi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Ehudi atamwalira, Aisraele adachitanso zinthu zoipira Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Ehudi atamwalira, Aisraeli anachitanso zinthu zoyipira Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Oweruza 4:1
12 Mawu Ofanana  

Yehova Inu, maso anu sali pachoonadi kodi? Munawapanda iwo, koma sanaphwetekedwe mtima; munawatha iwo, koma akana kudzudzulidwa; alimbitsa nkhope zao koposa mwala; akana kubwera.


Ndipo ndinene chiyaninso? Pakuti idzandiperewera nthawi ndifotokozere za Gideoni, Baraki, Samisoni, Yefita; za Davide, ndi Samuele ndi aneneri;


amene mwa chikhulupiriro anagonjetsa maufumu, anachita chilungamo, analandira malonjezano, anatseka pakamwa pa mikango,


Ndipo ana a Israele anaonjeza kuchita choipa pamaso pa Yehova, natumikira Abaala, ndi Aasitaroti, ndi milungu ya Aramu, ndi milungu ya Sidoni, ndi milungu ya Mowabu, ndi milungu ya ana a Amoni, ndi milungu ya Afilisti; ndipo anamleka Yehova osamtumikira.


Ndipo ana a Israele anachita choipa pamaso pa Yehova, natumikira Abaala;


Koma ana a Israele anaonjezanso kuchita choipa pamaso pa Yehova; pamenepo Yehova analimbitsa Egiloni mfumu ya Mowabu pa Israele, popeza anachita choipa pamaso pa Yehova.


Ndipo ana a Israele anachita choipa pamaso pa Yehova, naiwala Yehova Mulungu wao, natumikira Abaala ndi zifanizo.


Koma ana a Israele anachita choipa pamaso pa Yehova; ndipo Yehova anawapereka m'dzanja la Midiyani zaka zisanu ndi ziwiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa