Oweruza 4:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo ana a Israele anaonjeza kuchita choipa pamaso pa Yehova, atafa Ehudi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo ana a Israele anaonjeza kuchita choipa pamaso pa Yehova, atafa Ehudi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ehudi atamwalira, Aisraele adachitanso zinthu zoipira Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ehudi atamwalira, Aisraeli anachitanso zinthu zoyipira Yehova. Onani mutuwo |