Oweruza 3:3 - Buku Lopatulika3 anasiya mafumu asanu a Afilisti ndi Akanani onse, ndi Asidoni, ndi Ahivi okhala m'phiri la Lebanoni, kuyambira phiri la Baala-Heremoni mpaka polowera ku Hamati. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 anasiya mafumu asanu a Afilisti ndi Akanani onse, ndi Asidoni, ndi Ahivi okhala m'phiri la Lebanoni, kuyambira phiri la Baala-Heremoni mpaka polowera ku Hamati. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mitunduyo ndi iyi: mafumu asanu a Afilisti, Akanani onse, Asidoni onse ndi Ahivi amene ankakhala ku mapiri a Lebanoni, kuyambira ku phiri la Baala-Heremoni mpaka ku mpata wa Hamati. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mitundu ya anthuyo ndi: Mafumu asanu a Afilisti, Akanaani onse, Asidoni, ndi Ahivi amene ankakhala ku mapiri a Lebanoni kuyambira ku phiri la Baala-Herimoni mpaka ku Lebo Hamati. Onani mutuwo |
Pamenepo amuna asanuwa anachoka, nafika ku Laisi; naona anthu anali m'mwemo, kuti anakhala okhazikika mtima, monga anakhala Asidoni, odekha ndi osatekeseka; popeza m'dzikomo munalibe mwini bwalo wakuchititsa manyazi m'chinthu chilichonse; nasiyana kutali ndi Asidoni, ndipo analibe kanthu ndi munthu aliyense.