Oweruza 3:2 - Buku Lopatulika2 chifukwa chake ndicho chokha chakuti adziwitse mibadwo ya ana a Israele ndi kuwaphunzitsa nkhondo, ngakhale iwo okhaokha osaidziwa konse kale; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 chifukwa chake ndicho chokha chakuti adziwitse mibadwo ya ana a Israele ndi kuwaphunzitsa nkhondo, ngakhale iwo okhaokha osaidziwa konse kale; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Chauta ankangofuna kuti mibadwo yonse ya Aisraele idziŵe kumenya nkhondo, ndiponso kuti aphunzitse makamaka amene sadaidziŵe nkhondo nkale lonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 (Yehova anachita izi kuti Aisraeli onse aphunzire kumenya nkhondo; makamaka amene nʼkale lonse sanadziwe kumenya nkhondo. Onani mutuwo |