Oweruza 3:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo iyo ndiyo mitundu ya anthu anaisiyapo Yehova kuyesa nayo Israele, ndiwo onse amene sanadziwe nkhondo zonse za Kanani; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo iyo ndiyo mitundu ya anthu anaisiyapo Yehova kuyesa nayo Israele, ndiwo onse amene sanadziwe nkhondo zonse za Kanani; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsono Chauta adasiya mitundu ina ya anthu, kuti ayese nayo Aisraele, ndiye kuti Aisraele onse amene sadamenye nao nkhondo ku Kanani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Iyi ndi mitundu ya anthu yomwe Yehova anayisiya kuti ayese nayo Aisraeli amene sanadziwe kumenya nkhondo mu Kanaani Onani mutuwo |