Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Oweruza 2:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo Yoswa mwana wa Nuni, mtumiki wa Yehova anafa wa zaka zake zana ndi khumi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo Yoswa mwana wa Nuni, mtumiki wa Yehova anafa wa zaka zake zana ndi khumi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Yoswa, mwana wa Nuni, mtumiki wa Chauta, adamwalira ali ndi zaka 110.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Yoswa mwana wa Nuni, mtumiki wa Yehova, anamwalira ali ndi zaka 110.

Onani mutuwo Koperani




Oweruza 2:8
4 Mawu Ofanana  

Ndipo atafa Yoswa, ana a Israele anafunsira kwa Yehova ndi kuti, Adzayamba ndani kutikwerera pa Akanani kuwathira nkhondo?


Ndipo anthuwo anatumikira Yehova masiku onse a Yoswa, ndi masiku onse a akuluakulu otsala atafa Yoswa, amene adaona ntchito yaikulu yonse ya Yehova anaichitira Israele.


Ndipo anamuika m'malire a cholowa chake mu Timnati-Heresi, ku mapiri a Efuremu, kumpoto kwa phiri la Gaasi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa