Oweruza 2:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo kunali, pamene mthenga wa Yehova ananena mau awa kwa ana onse a Israele, anthuwo anakweza mau ao, nalira misozi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo kunali, pamene mthenga wa Yehova ananena mau awa kwa ana onse a Israele, anthuwo anakweza mau ao, nalira misozi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pamene mngelo wa Chauta adalankhula mau ameneŵa kwa Aisraele onse, anthuwo adayamba kufuula ndi kulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mngelo wa Mulungu atayankhula izi kwa Aisraeli, onse analira mokweza, Onani mutuwo |