Oweruza 2:2 - Buku Lopatulika2 ndipo inu, musamachita pangano ndi nzika za m'dziko ili; muzigamula maguwa ao a nsembe. Koma simunamvere mau anga; mwachichita ichi chifukwa ninji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 ndipo inu, musamachita pangano ndi nzika za m'dziko ili; muzigamula maguwa ao a nsembe. Koma simunamvera mau anga; mwachichita ichi chifukwa ninji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsono inuyo musadzachite chipangano ndi nzika za dziko lino. Mudzaphwanye maguwa ao onse.’ Koma inu simudamvere lamulo langa. Zimenezi mwachitiranji? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 ndipo inu musadzachite pangano ndi anthu a dziko lino, koma mudzaphwanye maguwa awo ansembe.’ Koma inu simunamvere lamulo langa. Chifukwa chiyani mwachita zimenezi? Onani mutuwo |