Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Oweruza 15:4 - Buku Lopatulika

4 Namuka Samisoni, nagwira ankhandwe mazana atatu, natenga miuni, nalunza michira, naika muuni pakati pa michira iwiri iliyonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Namuka Samisoni, nagwira ankhandwe mazana atatu, natenga miuni, nalunza michira, naika muuni pakati pa michira iwiri iliyonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Motero Samisoni adakagwira nkhandwe mazana atatu nazimangirira michira ziŵiriziŵiri. Kenaka pa mfundo iliyonse ya michirayo adamangirirapo nsakali naziyatsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Choncho Samsoni anapita nakagwira nkhandwe 300 nazimangirira michira ziwiriziwiri ndipo pa fundo iliyonse ya michirayo anamangirira nsakali.

Onani mutuwo Koperani




Oweruza 15:4
8 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake iye anati kwa anyamata ake, Onani munda wa Yowabu uli pafupi ndi wanga, ndipo iye ali ndi barele pamenepo, mukani mukamtenthere. Ndipo anyamata a Abisalomu anatentha za m'mundawo.


Adzawapereka kumphamvu ya lupanga; iwo adzakhala gawo la ankhandwe.


Monga woyaluka woponya nsakali, mivi, ndi imfa,


Mutigwirire ankhandwe, ngakhale aang'ono, amene akuononga minda yamipesa; pakuti m'minda yathu yamipesa muphuka biriwiri.


nukati kwa iye, Chenjera, khala ulipo; usaope, mtima wako usalefuke, chifukwa cha zidutswa ziwirizi za miuni yofuka, chifukwa cha mkwiyo waukali wa Rezini ndi Aramu, ndi wa mwana wa Remaliya.


paphiri la Ziyoni lopasukalo ankhandwe ayendapo.


Koma Samisoni, ananena nao, Nthawi ino ndikhala wosapalamula pa Afilisti, powachitira choipa ine.


Nayatsa miuni, nawataya ku tirigu wosacheka wa Afilisti, natentha miulu, ndi tirigu wosacheka yemwe, ndi minda ya azitona yomwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa