Oweruza 15:3 - Buku Lopatulika3 Koma Samisoni, ananena nao, Nthawi ino ndikhala wosapalamula pa Afilisti, powachitira choipa ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Koma Samisoni, ananena nao, Nthawi yino ndikhala wosapalamula pa Afilisti, powachitira choipa ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Samisoni adaŵauza kuti, “Ulendo uno aliyense asandinene, ndikaŵachita choipa chachikulu Afilistiŵa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Samsoni anawawuza kuti, “Pano sindikhala wochimwa ndikawachita choyipa chachikulu Afilistiwa.” Onani mutuwo |