Oweruza 13:8 - Buku Lopatulika8 Pamenepo Manowa anapembedza Yehova, nati, Yehova, ndikupemphani, atidzerenso munthu wa Mulungu mudamtumayo, natilangize icho tizichitira mwanayo akadzabadwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Pamenepo Manowa anapembedza Yehova, nati, Yehova, ndikupemphani, atidzerenso munthu wa Mulungu mudamtumayo, natilangize icho tizichitira mwanayo akadzabadwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Tsono Manowa adapemphera kwa Chauta kuti, “Inu Chauta, ndapota nanu, mulole kuti munthu amene mudaamtuma uja abwerenso, adzatiphunzitse zimene tiyenera kuchita naye mnyamata amene adzabadweyo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Kenaka Manowa anapemphera kwa Yehova kuti, “Chonde Ambuye, lolani munthu wa Mulungu amene munamutuma abwerenso kwa ife kuti adzatiphunzitse zochita ndi mwanayo akadzabadwa.” Onani mutuwo |