Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Oweruza 13:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo panali munthu wina wa Zora wa banja la Adani, dzina lake ndiye Manowa; ndi mkazi wake analibe mwana, sanabale.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo panali munthu wina wa Zora wa banja la Adani, dzina lake ndiye Manowa; ndi mkazi wake analibe mwana, sanabala.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Ku Zora kunali munthu wina, wa fuko la Dani, dzina lake Manowa. Mkazi wake analibe ana, anali wosabereka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Ku Zora kunali munthu wina dzina lake Manowa, wochokera ku fuko la Dani. Mkazi wake analibe ana popeza anali wosabereka.

Onani mutuwo Koperani




Oweruza 13:2
10 Mawu Ofanana  

Koma Sarai anali wouma; analibe mwana.


Ndipo Sarai mkazi wake wa Abramu sanambalire iye mwana; ndipo anali ndi mdzakazi, wa ku Ejipito, dzina lake Hagara.


Ndipo Isaki anampembedzera mkazi wake kwa Yehova popeza anali wouma: ndipo Yehova analola kupembedza kwake, ndipo Rebeka mkazi wake anatenga pakati.


Dani adzaweruza anthu ake, monga limodzi la mafuko a Israele.


Ndi mabanja a Kiriyati-Yearimu: Aitiri, ndi Aputi, ndi Asumati, ndi Amisrai; Azorati ndi Aestaoli anafuma kwa iwowa.


Ndipo analibe mwana, popeza Elizabeti anali wouma, ndipo onse awiri anakalamba.


Ku chigwa, Esitaoli, ndi Zora ndi Asina;


Ndipo malire a cholowa chao anali Zora, ndi Esitaoli, ndi Irisemesi;


Ndipo mthenga wa Yehova anakwera kuchokera ku Giligala kunka ku Bokimu. Ndipo anati, Ndinakukweretsani kuchokera ku Ejipito, ndi kulowetsa inu m'dziko limene ndinalumbirira makolo anu; ndipo ndinati, Sindidzathyola chipangano changa nanu ku nthawi yonse;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa