Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Oweruza 13:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo mkaziyo anafulumira nathamanga, nauza mwamuna wake, nanena naye, Taona, wandionekera munthu anandidzerayo tsiku lija.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo mkaziyo anafulumira nathamanga, nauza mwamuna wake, nanena naye, Taona, wandionekera munthu anandidzerayo tsiku lija.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Mkazi uja adathamanga nakauza mwamuna wake kuti, “Munthu uja adaabwera kuno tsiku lijaliyu wandiwonekeranso.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Tsono mkaziyo anathamanga kukawuza mwamuna wake kuti, “Wandionekeranso munthu uja amene anabwera kwa ine tsiku lija.”

Onani mutuwo Koperani




Oweruza 13:10
4 Mawu Ofanana  

Pamenepo anadza mkaziyo, nanena ndi mwamuna wake ndi kuti, Wandidzera munthu wa Mulungu; maonekedwe ake ndiwo ngati maonekedwe a mthenga wa Mulungu oopsa ndithu; ndipo sindinamfunse uko achokera kapena sanandiuzenso dzina lake;


Ndipo Mulungu anamvera mau a Manowa; ndi mthenga wa Mulungu anamdzeranso mkaziyo, pamene anali m'munda, mwamuna wake Manowa palibe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa