Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Oweruza 11:6 - Buku Lopatulika

6 nati kwa Yefita, Tiye ukhale kazembe wathu kuti tilimbane ndi ana a Amoni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 nati kwa Yefita, Tiye ukhale kazembe wathu kuti tilimbane ndi ana a Amoni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Akuluakuluwo adauza Yefita kuti, “Bwera udzakhale mtsogoleri wathu kuti timenyane nawo nkhondo Aamoni.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Iwo anati kwa iye, “Bwera ukhale mkulu wathu wankhondo kuti timenyane ndi Amoni.”

Onani mutuwo Koperani




Oweruza 11:6
4 Mawu Ofanana  

Pamene mwamuna adzamgwira mbale wake m'nyumba ya atate wake, nadzati, Iwe uli ndi chovala, khala wolamulira wathu, ndi kupasula kumeneku kukhale m'dzanja lako;


Ndipo ana a Amoni analalikiridwa, namanga misasa mu Giliyadi. Ndi ana a Israele anasonkhana namanga misasa ku Mizipa.


ndipo kunatero, pamene ana a Amoni anathira nkhondo pa Israele, akulu a Giliyadi anamuka kutenga Yefita m'dziko la Tobu;


Ndipo Yefita anati kwa akulu a Giliyadi, Simunandide kodi, ndi kundichotsa m'nyumba ya atate wanga? Ndipo mundidzeranji tsopano pokhala muli m'kusauka?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa