Oweruza 11:1 - Buku Lopatulika1 Yefita Mgiliyadi ndipo anali ngwazi yamphamvu, ndiye mwana wa mkazi wadama; koma Giliyadi adabala Yefita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Yefita Mgiliyadi ndipo anali ngwazi yamphamvu, ndiye mwana wa mkazi wadama; koma Giliyadi adabala Yefita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Yefita wa ku Giliyadi anali wankhondo wamphamvu. Bambo wake anali Giliyadi, mai wake anali mkazi wadama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yefita wa ku Giliyadi anali wankhondo wa mphamvu. Iyeyu amayi ake anali mkazi wachiwerewere, ndipo abambo ake anali Giliyadi. Onani mutuwo |