Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Oweruza 10:5 - Buku Lopatulika

5 Nafa Yairi, naikidwa mu Kamoni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Nafa Yairi, naikidwa m'Kamoni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Pambuyo pake Yairo adamwalira, naikidwa ku Kamoni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Atamwalira Yairi anayikidwa mʼmanda ku Kamoni.

Onani mutuwo Koperani




Oweruza 10:5
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anali nao ana aamuna makumi atatu okwera pa ana a abulu makumi atatu, iwo ndipo anali nayo mizinda makumi atatu, otchedwa midzi ya Yairi, mpaka lero lino, ndiyo m'dziko la Giliyadi.


Ndipo ana a Israele anaonjeza kuchita choipa pamaso pa Yehova, natumikira Abaala, ndi Aasitaroti, ndi milungu ya Aramu, ndi milungu ya Sidoni, ndi milungu ya Mowabu, ndi milungu ya ana a Amoni, ndi milungu ya Afilisti; ndipo anamleka Yehova osamtumikira.


Ndipo anaphwanya napsinja ana a Israele chaka chija, natero ndi ana onse a Israele okhala tsidya lija la Yordani m'dziko la Aamori, ndilo Giliyadi, zaka khumi ndi zisanu ndi zitatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa