Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Oweruza 10:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo anaweruza Israele zaka makumi awiri ndi zitatu, nafa, naikidwa mu Samiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo anaweruza Israele zaka makumi awiri ndi zitatu, nafa, naikidwa m'Samiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Adaweruza Aisraele zaka 23. Pambuyo pake adamwalira, naikidwa ku Samiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Iye anatsogolera Aisraeli kwa zaka 23, ndipo anamwalira ndi kuyikidwa ku Samiri.

Onani mutuwo Koperani




Oweruza 10:2
3 Mawu Ofanana  

Atafa Abimeleki, anauka kupulumutsa Israele Tola mwana wa Puwa, mwana wa Dodo munthu wa Isakara; nakhala iye mu Samiri ku mapiri a Efuremu.


Atafa iye, anauka Yairi Mgiliyadi, naweruza Israele zaka makumi awiri mphambu ziwiri.


Pokhala Israele mu Hesiboni ndi midzi yake, ndi mu Aroere ndi midzi yake ndi m'mizinda yonse yokhala m'mphepete mwa Arinoni zaka mazana atatu; munalekeranji kulandanso nthawi ija?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa