Oweruza 1:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo atatero ana a Yuda anatsika kuthirana nao nkhondo Akanani akukhala kumapiri, ndi kumwera ndi kuchidikha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo atatero ana a Yuda anatsika kuthirana nao nkhondo Akanani akukhala kumapiri, ndi kumwera ndi kuchidikha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Kenaka Ayudawo adapita kukamenyana ndi Akanani amene ankakhala m'dziko lamapiri, m'dziko la Negebu lakumwera, ndiponso m'zigwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Kenaka Ayuda anapita kukamenyana ndi Akanaani omwe amakhala ku dziko la ku mapiri, dziko la Negevi kummwera ndiponso mu zigwa. Onani mutuwo |