Oweruza 1:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo atafa Yoswa, ana a Israele anafunsira kwa Yehova ndi kuti, Adzayamba ndani kutikwerera pa Akanani kuwathira nkhondo? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo atafa Yoswa, ana a Israele anafunsira kwa Yehova ndi kuti, Adzayamba ndani kutikwerera pa Akanani kuwathira nkhondo? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Yoswa atafa, Aisraele adafunsa Chauta kuti, “Ndani mwa ife amene ayambe kulimbana ndi Akanani, kumenyana nawo nkhondo?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Atamwalira Yoswa Aisraeli anafunsa Yehova kuti, “Ndani mwa ife ayambe nkhondo yomenyana ndi Akanaani?” Onani mutuwo |