Numeri 7:50 - Buku Lopatulika50 chipande chimodzi chagolide cha masekeli khumi, chodzala ndi chofukiza; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201450 chipande chimodzi chagolide cha masekeli khumi, chodzala ndi chofukiza; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa50 Adaperekanso kambale kamodzi kagolide ka magaramu 110, kodzaza ndi lubani, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero50 mbale imodzi yagolide yolemera magalamu 110, yodzaza ndi lubani; Onani mutuwo |