Numeri 35:26 - Buku Lopatulika26 Koma wakupha munthu akatuluka nthawi iliyonse kulumpha malire a mzinda wake wopulumukirako kumene anathawirako; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Koma wakupha munthu akatuluka nthawi iliyonse kulumpha malire a mudzi wake wopulumukirako kumene anathawirako; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Koma ngati munthu wopha mnzake mwangoziyo atuluka nthaŵi iliyonse kunja kwa malire a mzinda umene adathaŵiramo, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 “ ‘Koma ngati wolakwayo atuluka kunja kwa malire a mzinda wopulumukirako kumene anathawira Onani mutuwo |